1 Kale Efereimu ankati akayankhula, anthu ankanjenjemera;
2 Tsopano akunka nachimwirachimwirabe;
3 Choncho adzakhala ngati nkhungu yammawa,
4 Koma Ine ndine Yehova Mulungu wanu,
5 Ndinakusamalira mʼchipululu,
6 Pamene ndinawadyetsa, iwo anakhuta;
7 Motero ndidzawalumphira ngati mkango,
8 Ngati chimbalangondo cholandidwa ana ake,
9 “Iwe Israeli, wawonongedwa,
10 Kodi mfumu yako ili kuti, kuti ikupulumutse?
11 Choncho Ine ndinakupatsani mfumu mwachipseramtima,
12 Kulakwa kwa Efereimu kwasungidwa,
13 Zowawa zonga za mayi pa nthawi yobala mwana zamugwera,
14 “Ndidzawapulumutsa ku mphamvu ya manda;
15 ngakhale Efereimu akondwe pakati pa abale ake,
16 Anthu a ku Samariya adzalangidwa chifukwa cha zolakwa zawo,