Joel 1

NYA

1 Yehova anayankhula ndi Yoweli mwana wa Petueli.

2 Inu akuluakulu, imvani izi;

3 Muwafotokozere ana anu,

4 Chimene dzombe losamera mapiko lasiya

5 Dzukani, inu zidakwa ndipo mulire!

6 Mtundu wa anthu wathira nkhondo dziko langa,

7 Wawononga mphesa zanga

8 Lirani ngati namwali wovala chiguduli,

9 Chopereka cha chakudya ndi cha chakumwa

10 Minda yaguga,

11 Khalani ndi nkhawa, inu alimi,

12 Mpesa wauma

13 Inu ansembe, valani ziguduli ndipo lirani;

14 Lengezani tsiku lopatulika losala zakudya,

15 Kalanga ine tsikulo!

16 Kodi chakudya chathu sichachotsedwa

17 Mbewu zikunyala

18 Taonani mmene zikulirira ziweto;

19 Kwa Inu Yehova ndilirira,

20 Ngakhale nyama zakuthengo zikulirira Inu;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado