1 Yehova anayankhula ndi Yoweli mwana wa Petueli.
2 Inu akuluakulu, imvani izi;
3 Muwafotokozere ana anu,
4 Chimene dzombe losamera mapiko lasiya
5 Dzukani, inu zidakwa ndipo mulire!
6 Mtundu wa anthu wathira nkhondo dziko langa,
7 Wawononga mphesa zanga
8 Lirani ngati namwali wovala chiguduli,
9 Chopereka cha chakudya ndi cha chakumwa
10 Minda yaguga,
11 Khalani ndi nkhawa, inu alimi,
12 Mpesa wauma
13 Inu ansembe, valani ziguduli ndipo lirani;
14 Lengezani tsiku lopatulika losala zakudya,
15 Kalanga ine tsikulo!
16 Kodi chakudya chathu sichachotsedwa
17 Mbewu zikunyala
18 Taonani mmene zikulirira ziweto;
19 Kwa Inu Yehova ndilirira,
20 Ngakhale nyama zakuthengo zikulirira Inu;