1 Lizani lipenga mu Ziyoni.
2 tsiku la mdima ndi chisoni,
3 Patsogolo pawo moto ukupsereza,
4 Maonekedwe awo ali ngati akavalo;
5 Akulumpha pamwamba pa mapiri
6 Akangowaona, anthu a mitundu ina amazunzika mu mtima;
7 Amathamanga ngati ankhondo;
8 Iwo sakankhanakankhana,
9 Amakhamukira mu mzinda,
10 Patsogolo pawo dziko limagwedezeka,
11 Yehova amabangula
12 “Ngakhale tsopano,
13 Ngʼambani mtima wanu
14 Akudziwa ndani? Mwina adzasintha maganizo nʼkutimvera chisoni,
15 Lizani lipenga mu Ziyoni,
16 Sonkhanitsani anthu pamodzi,
17 Ansembe amene amatumikira pamaso pa Yehova,
18 Pamenepo Yehova adzachitira nsanje dziko lake
19 Yehova adzawayankha kuti,
20 “Ine ndidzachotsa ankhondo akumpoto kuti apite kutali ndi inu,
21 Iwe dziko usachite mantha;
22 Inu nyama zakuthengo, musachite mantha,
23 Inu anthu a ku Ziyoni sangalalani,
24 Pa malo opunthira padzaza tirigu;
25 “Ine ndidzakubwezerani zonse zimene zinawonongedwa ndi dzombe,
26 Mudzakhala ndi chakudya chambiri, mpaka mudzakhuta,
27 Pamenepo inu mudzadziwa kuti Ine ndili mu Israeli,
28 “Ndipo patapita nthawi,
29 Ngakhalenso pa antchito anga aamuna ndi aakazi
30 Ndidzaonetsa zodabwitsa mlengalenga
31 Dzuwa lidzadetsedwa
32 Ndipo aliyense amene adzayitana