1 Mʼmasiku otsiriza,
2 Mayiko ambiri adzabwera ndikunena kuti,
3 Iye adzaweruza pakati pa anthu amitundu yambiri
4 Munthu aliyense adzakhala pansi pa tsinde pa mtengo wake wa mpesa
5 Mitundu yonse ya anthu
6 “Tsiku limenelo, Yehova akuti,
7 Anthu olumalawo ndidzawasandutsa anthu anga otsala.
8 Kunena za iwe, nsanja ya ziweto zanga,
9 Chifukwa chiyani tsopano ukulira mofuwula,
10 Gubuduka ndi ululu, iwe mwana wamkazi wa Ziyoni,
11 Koma tsopano mitundu yambiri ya anthu
12 Koma iwo sakudziwa
13 “Imirira, puntha, iwe mwana wamkazi wa Ziyoni,