1 Ndipo ine ndinati,
2 inu amene mumadana ndi zabwino ndi kukonda zoyipa;
3 inu amene mumadya anthu anga,
4 Pamenepo adzalira kwa Yehova,
5 Yehova akuti,
6 Nʼchifukwa chake kudzakuderani,
7 Alosi adzachita manyazi
8 Koma kunena za ine, ndadzazidwa ndi mphamvu,
9 Imvani izi, inu atsogoleri a nyumba ya Yakobo,
10 inu amene mukumanga Ziyoni pokhetsa magazi,
11 Atsogoleri ake amalandira chiphuphu kuti aweruze,
12 Choncho chifukwa cha inu,