1 Tsoka kwa amene amakonzekera chiwembu,
2 Amasirira minda ndi kuyilanda,
3 Nʼchifukwa chake Yehova akuti,
4 Tsiku limenelo anthu adzakuchitani chipongwe;
5 Nʼchifukwa chake simudzakhala ndi munthu mu msonkhano wa Yehova
6 Aneneri awo amanena kuti, “Usanenere!
7 Inu nyumba ya Yakobo, monga zimenezi ndi zoyenera kuzinena:
8 Posachedwapa anthu anga andiwukira
9 Mumatulutsa akazi a anthu anga
10 Nyamukani, chokani!
11 Ngati munthu wabodza ndi wachinyengo abwera nʼkunena kuti,
12 “Inu banja la Yakobo, ndidzakusonkhanitsani nonse;
13 Amene adzawapulumutse adzayenda patsogolo pawo;