1 Yehova anayankhula ndi Mika wa ku Moreseti pa nthawi ya ulamuliro wa Yotamu, Ahazi ndi Hezekiya, mafumu a ku Yuda. Awa ndi masomphenya amene iye anaona onena za Samariya ndi Yerusalemu.
2 Tamverani, inu anthu a mitundu yonse,
3 Taonani! Yehova akubwera kuchokera ku malo ake;
4 Mapiri akusungunuka pansi pake,
5 Zonsezi ndi chifukwa cha cholakwa cha Yakobo,
6 “Choncho Ine ndidzasandutsa Samariya kukhala bwinja,
7 Mafano ake onse ndidzawaphwanyaphwanya;
8 Chifukwa cha zimenezi ine ndidzalira momvetsa chisoni;
9 Pakuti chilonda cha Samariya nʼchosachizika;
10 Musanene zimenezi ku Gati;
11 Inu anthu okhala ku Safiro,
12 Anthu amene amakhala ku Maroti akubuwula ndi ululu,
13 Inu anthu okhala ku Lakisi
14 Chifukwa chake perekani mphatso zolawirana
15 Ndidzabweretsa mgonjetsi kudzalimbana ndi inu
16 Metani mipala mitu yanu kuonetsa kuti mukulirira