1 Haa! Golide wathimbirira,
2 Haa! Ana a Ziyoni amtengowapatali
3 Ngakhale nkhandwe zimapereka bere
4 Lilime la mwana lakangamira kukhosi
5 Iwo amene kale ankadya zonona
6 Kuyipa kwa anthu anga kunali kwakukulu
7 Akalonga ake anali owala koposa chisanu chowundana
8 Koma tsopano maonekedwe awo ndi akuda kuposa mwaye;
9 Amene anaphedwa ndi lupanga aliko bwino kuposa
10 Amayi achifundo afika
11 Yehova wakwaniritsa ukali wake;
12 Mafumu a pa dziko lapansi sanakhulupirire,
13 Koma izi zinachitika chifukwa cha kuchimwa kwa aneneri ake
14 Tsopano akungoyendayenda mʼmisewu ya mu mzinda
15 Anthu akuwafuwulira kuti, “Chokani! Inu anthu odetsedwa!”
16 Yehova mwini wake wawabalalitsa;
17 Ndiponso maso athu atopa nʼkuyangʼana,
18 Anthu ankalondola mapazi athu,
19 Otilondola akuthamanga kwambiri
20 Wodzozedwa wa Yehova, mpweya wathu wotipatsa moyo,
21 Kondwera ndi kusangalala, mwana wamkazi wa Edomu.
22 Iwe mwana wamkazi wa Ziyoni, chilango chako chidzatha;