Lamentações 3

NYA

1 Ine ndine munthu amene ndaona masautso

2 Wandipititsa kutali ndipo wandiyendetsa

3 zoonadi anandikantha ndi dzanja lake

4 Wakalambitsa khungu langa ndi mnofu wanga,

5 Wandizinga ndi kundizungulira

6 Wandikhazika mu mdima

7 Wandimangira khoma kotero kuti sindingathawe,

8 Ngakhale pamene ndifuwula kapena kupempha chithandizo,

9 Wanditsekera njira yanga ndi miyala yosema;

10 Wandidikirira ngati chimbalangondo,

11 Wandikokera pambali ndi kundingʼambangʼamba,

12 Wakoka uta wake

13 Walasa mtima wanga

14 Ndinakhala choseketsa cha anthu anga onse;

15 Wandidyetsa zowawa

16 Wathyola mano anga ndi miyala;

17 Wandichotsera mtendere;

18 Choncho ndikuti, “Ulemerero wanga wachoka

19 Kukumbukira masautso anga ndi kusowa pokhala,

20 Ine ndikuzikumbukira bwino izi,

21 Komabe ndimakumbukira zimenezi,

22 Ife sitinawonongekeretu chifukwa chikondi cha Yehova ndi chachikulu,

23 Zimaoneka zatsopano mmawa uliwonse;

24 Mu mtima mwanga ndimati, “Yehova ndiye zanga zonse;

25 Yehova ndi wabwino kwa amene amayembekezera Iye,

26 nʼkwabwino kudikira chipulumutso cha

27 Nʼkwabwino kuti munthu asenze goli

28 Akhale chete pa yekha,

29 Abise nkhope yake mʼfumbi

30 Apereke tsaya lake kwa iye amene angamumenye,

31 Chifukwa Ambuye satayiratu

32 Ngakhale amabweretsa zowawa, Iye adzawachitira chifundo,

33 Pakuti sabweretsa masautso mwadala,

34 Kuphwanya ndi phazi

35 kukaniza munthu ufulu wake

36 kumana munthu chiweruzo cholungama—

37 Kodi ndani angayankhule zinthu nʼkuchitika

38 Kodi zovuta ndi zabwino sizituluka

39 Kodi nʼchifukwa chiyani munthu aliyense wamoyo amadandaula

40 Tiyeni tisanthule ndi kuyesa njira zathu,

41 Tiyeni tikweze mitima yathu ndi manja athu

42 “Ife tachimwa ndi kuwukira

43 “Mwadzikuta ndi mkwiyo ndi kutilondola ndipo

44 Mwadzikuta mu mtambo

45 Mwatisandutsa zinyatsi ndi zinyalala

46 “Adani anthu atitsekulira pakamwa.

47 Ife tadzazidwa ndi mantha pakuti tagwa mʼdzenje,

48 Misozi mʼmaso mwanga ikungoti mbwembwembwe

49 Misozi idzatsika kosalekeza,

50 mpaka Yehova ayangʼane pansi

51 Mtima wanga ukupweteka poona zimenezi

52 Akundisaka ngati mbalame,

53 Ayesa kundipha pondiponya mʼdzenje

54 madzi anamiza mutu wanga

55 Ndinayitana dzina lanu Inu Yehova,

56 Inu munamva kudandaula kwanga. “Mundimvere

57 Munafika pafupi pamene ndinakuyitanani,

58 Inu Ambuye munandiwombola ku mlandu wanga;

59 Yehova, mwaona zoyipa zimene andichitira.

60 Mwaona kuzama kwa kubwezera kwawo,

61 Inu Yehova mwamva kunyoza kwawo,

62 manongʼonongʼo a adani anga

63 Tawaonani! Kaya ali pansi kapena kuyimirira,

64 Inu Yehova, muwabwezere chowayenera,

65 Phimbani mitima yawo,

66 Muwalondole mwaukali ndipo

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado