1 Ine ndine munthu amene ndaona masautso
2 Wandipititsa kutali ndipo wandiyendetsa
3 zoonadi anandikantha ndi dzanja lake
4 Wakalambitsa khungu langa ndi mnofu wanga,
5 Wandizinga ndi kundizungulira
6 Wandikhazika mu mdima
7 Wandimangira khoma kotero kuti sindingathawe,
8 Ngakhale pamene ndifuwula kapena kupempha chithandizo,
9 Wanditsekera njira yanga ndi miyala yosema;
10 Wandidikirira ngati chimbalangondo,
11 Wandikokera pambali ndi kundingʼambangʼamba,
12 Wakoka uta wake
13 Walasa mtima wanga
14 Ndinakhala choseketsa cha anthu anga onse;
15 Wandidyetsa zowawa
16 Wathyola mano anga ndi miyala;
17 Wandichotsera mtendere;
18 Choncho ndikuti, “Ulemerero wanga wachoka
19 Kukumbukira masautso anga ndi kusowa pokhala,
20 Ine ndikuzikumbukira bwino izi,
21 Komabe ndimakumbukira zimenezi,
22 Ife sitinawonongekeretu chifukwa chikondi cha Yehova ndi chachikulu,
23 Zimaoneka zatsopano mmawa uliwonse;
24 Mu mtima mwanga ndimati, “Yehova ndiye zanga zonse;
25 Yehova ndi wabwino kwa amene amayembekezera Iye,
26 nʼkwabwino kudikira chipulumutso cha
27 Nʼkwabwino kuti munthu asenze goli
28 Akhale chete pa yekha,
29 Abise nkhope yake mʼfumbi
30 Apereke tsaya lake kwa iye amene angamumenye,
31 Chifukwa Ambuye satayiratu
32 Ngakhale amabweretsa zowawa, Iye adzawachitira chifundo,
33 Pakuti sabweretsa masautso mwadala,
34 Kuphwanya ndi phazi
35 kukaniza munthu ufulu wake
36 kumana munthu chiweruzo cholungama—
37 Kodi ndani angayankhule zinthu nʼkuchitika
38 Kodi zovuta ndi zabwino sizituluka
39 Kodi nʼchifukwa chiyani munthu aliyense wamoyo amadandaula
40 Tiyeni tisanthule ndi kuyesa njira zathu,
41 Tiyeni tikweze mitima yathu ndi manja athu
42 “Ife tachimwa ndi kuwukira
43 “Mwadzikuta ndi mkwiyo ndi kutilondola ndipo
44 Mwadzikuta mu mtambo
45 Mwatisandutsa zinyatsi ndi zinyalala
46 “Adani anthu atitsekulira pakamwa.
47 Ife tadzazidwa ndi mantha pakuti tagwa mʼdzenje,
48 Misozi mʼmaso mwanga ikungoti mbwembwembwe
49 Misozi idzatsika kosalekeza,
50 mpaka Yehova ayangʼane pansi
51 Mtima wanga ukupweteka poona zimenezi
52 Akundisaka ngati mbalame,
53 Ayesa kundipha pondiponya mʼdzenje
54 madzi anamiza mutu wanga
55 Ndinayitana dzina lanu Inu Yehova,
56 Inu munamva kudandaula kwanga. “Mundimvere
57 Munafika pafupi pamene ndinakuyitanani,
58 Inu Ambuye munandiwombola ku mlandu wanga;
59 Yehova, mwaona zoyipa zimene andichitira.
60 Mwaona kuzama kwa kubwezera kwawo,
61 Inu Yehova mwamva kunyoza kwawo,
62 manongʼonongʼo a adani anga
63 Tawaonani! Kaya ali pansi kapena kuyimirira,
64 Inu Yehova, muwabwezere chowayenera,
65 Phimbani mitima yawo,
66 Muwalondole mwaukali ndipo