1 Haa, Ambuye waphimba mwana wamkazi wa Ziyoni
2 Ambuye anawononga midzi yonse ya Yakobo mopanda chifundo;
3 Atakwiya kwambiri, Ambuye anathyola
4 Wakokera uta wake pa ife ngati ndife adani;
5 Ambuye ali ngati mdani;
6 Wagwetsa malo ake okhalamo ngati khumbi la mʼmunda;
7 Ambuye wakana guwa lake la nsembe
8 Yehova anatsimikiza kugwetsa
9 Zipata za Yerusalemu zalowa pansi;
10 Akuluakulu a mwana wamkazi wa Ziyoni
11 Maso anga atopa ndi kulira,
12 Anawo akufunsa amayi awo kuti,
13 Ndinganene chiyani za iwe?
14 Masomphenya a aneneri ako
15 Onse oyenda mʼnjira yako
16 Adani ako onse akutsekulira pakamwa ndi kukunyoza;
17 Yehova wachita chimene anakonzeratu;
18 Mitima ya anthu
19 Dzuka, fuwula usiku,
20 Inu Yehova, onani, ndipo ganizirani:
21 Anyamata ndi okalamba aligone pamodzi
22 Ngati momwe mumayitanira pa tsiku la phwando,