1 Haa! Mzinda uja wasiyidwa wokhawokha,
2 Ukulira mowawidwa mtima usiku wonse,
3 Yuda watengedwa ku ukapolo,
4 Misewu yopita ku Ziyoni ikulira,
5 Adani ake asanduka mabwana ake;
6 Ulemerero wonse wa mwana wamkazi wa Ziyoni
7 Pa masiku a masautso ndi kuzunzika kwake,
8 Yerusalemu wachimwa kwambiri
9 Uve wake umaonekera pa zovala zake;
10 Adani amulanda
11 Anthu ake onse akubuwula
12 “Kodi zimenezi mukuziyesa zachabe, inu nonse mukudutsa?
13 “Anatumiza moto kuchokera kumwamba,
14 “Wazindikira machimo anga onse
15 “Ambuye wakana
16 “Chifukwa cha zimenezi ndikulira
17 “Ziyoni wakweza manja ake,
18 “Yehova ndi wolungama,
19 “Ndinayitana abwenzi anga
20 “Inu Yehova, onani mmene ine ndavutikira!
21 “Anthu amva kubuwula kwanga,
22 “Lolani kuti ntchito zawo zoyipa zifike pamaso panu;