Lamentações 1

NYA

1 Haa! Mzinda uja wasiyidwa wokhawokha,

2 Ukulira mowawidwa mtima usiku wonse,

3 Yuda watengedwa ku ukapolo,

4 Misewu yopita ku Ziyoni ikulira,

5 Adani ake asanduka mabwana ake;

6 Ulemerero wonse wa mwana wamkazi wa Ziyoni

7 Pa masiku a masautso ndi kuzunzika kwake,

8 Yerusalemu wachimwa kwambiri

9 Uve wake umaonekera pa zovala zake;

10 Adani amulanda

11 Anthu ake onse akubuwula

12 “Kodi zimenezi mukuziyesa zachabe, inu nonse mukudutsa?

13 “Anatumiza moto kuchokera kumwamba,

14 “Wazindikira machimo anga onse

15 “Ambuye wakana

16 “Chifukwa cha zimenezi ndikulira

17 “Ziyoni wakweza manja ake,

18 “Yehova ndi wolungama,

19 “Ndinayitana abwenzi anga

20 “Inu Yehova, onani mmene ine ndavutikira!

21 “Anthu amva kubuwula kwanga,

22 “Lolani kuti ntchito zawo zoyipa zifike pamaso panu;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado