Jeremias 50

NYA

1 Uthenga umene Yehova anayankhula ndi mneneri Yeremiya wonena za mzinda wa Babuloni ndi anthu ake ndi uwu:

2 “Lengeza ndi kulalika pakati pa anthu a mitundu ina,

3 Mtundu wa anthu wochokera kumpoto wadzathira nkhondo Babuloni

4 “Masiku amenewo, nthawi imeneyo,”

5 Adzafunsa njira ya ku Ziyoni

6 “Anthu anga ali ngati nkhosa zotayika;

7 Aliyense amene anawapeza anawawononga;

8 “Thawaniko ku Babuloni;

9 Taonani, ndidzaukitsa gulu lankhondo lamphamvu la mitundu ina

10 Motero Ababuloni adzafunkhidwa;

11 “Inu Ababuloni, munawononga anthu anga osankhika.

12 Koma mzinda wanu udzachititsidwa manyazi kwambiri.

13 Chifukwa cha mkwiyo wa Yehova Babuloni adzakhala wopanda anthu

14 “Inu okoka uta,

15 Mufuwulireni mbali zonse pakuti wagonja.

16 Chotsani ku Babuloni munthu wofesa mbewu aliyense,

17 “Aisraeli ali ngati nkhosa zomwe zabalalika

18 Nʼchifukwa chake Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli akuti,

19 Koma ndidzabwezera Israeli ku msipu wake

20 Masiku amenewo, nthawi imeneyo,”

21 “Lithireni nkhondo dziko la Merataimu

22 Mʼdziko muli phokoso la nkhondo,

23 Taonani mʼmene waphwanyikira ndi kuwonongekera

24 Ndinakutchera msampha, iwe Babuloni,

25 Yehova watsekula nyumba ya zida zake

26 Mumenyane naye Babuloni mbali zonse.

27 Iphani ankhondo ake onse.

28 Tikumva anthu othawa nkhondo ochokera ku Babuloni

29 “Itanani anthu oponya mivi kudzathira nkhondo Babuloni.

30 Nʼchifukwa chake, anyamata ake adzaphedwa mʼmabwalo ake;

31 “Taona, ndikukuthira nkhondo, iwe wodzikuzawe,”

32 Wodzikuzawe udzapunthwa nʼkugwa

33 Yehova Wamphamvuzonse akuti,

34 Koma Mpulumutsi wawo ndi wamphamvu;

35 Yehova akuti,

36 Imfa yalunjika pa aneneri abodza

37 Imfa ilunjike pa akavalo ake ndi magaleta ake.

38 Chilala chilunjike pa madzi ake

39 “Nʼchifukwa chake nyama zakuthengo ndi afisi zidzakhala kumeneko

40 Monga momwe Mulungu anawonongera Sodomu ndi Gomora

41 “Taonani! Gulu lankhondo likubwera kuchokera kumpoto;

42 Atenga mauta ndi mikondo;

43 Mfumu ya ku Babuloni yamva za mbiri yawo,

44 Taonani, monga mkango wochokera ku nkhalango ya ku Yorodani

45 Nʼchifukwa chake imvani.

46 Akadzagwa Babuloni padzakhala mfuwu waukulu ndipo dziko lapansi lidzanjenjemera,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado