1 Uthenga umene Yehova anayankhula ndi mneneri Yeremiya wonena za mzinda wa Babuloni ndi anthu ake ndi uwu:
2 “Lengeza ndi kulalika pakati pa anthu a mitundu ina,
3 Mtundu wa anthu wochokera kumpoto wadzathira nkhondo Babuloni
4 “Masiku amenewo, nthawi imeneyo,”
5 Adzafunsa njira ya ku Ziyoni
6 “Anthu anga ali ngati nkhosa zotayika;
7 Aliyense amene anawapeza anawawononga;
8 “Thawaniko ku Babuloni;
9 Taonani, ndidzaukitsa gulu lankhondo lamphamvu la mitundu ina
10 Motero Ababuloni adzafunkhidwa;
11 “Inu Ababuloni, munawononga anthu anga osankhika.
12 Koma mzinda wanu udzachititsidwa manyazi kwambiri.
13 Chifukwa cha mkwiyo wa Yehova Babuloni adzakhala wopanda anthu
14 “Inu okoka uta,
15 Mufuwulireni mbali zonse pakuti wagonja.
16 Chotsani ku Babuloni munthu wofesa mbewu aliyense,
17 “Aisraeli ali ngati nkhosa zomwe zabalalika
18 Nʼchifukwa chake Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli akuti,
19 Koma ndidzabwezera Israeli ku msipu wake
20 Masiku amenewo, nthawi imeneyo,”
21 “Lithireni nkhondo dziko la Merataimu
22 Mʼdziko muli phokoso la nkhondo,
23 Taonani mʼmene waphwanyikira ndi kuwonongekera
24 Ndinakutchera msampha, iwe Babuloni,
25 Yehova watsekula nyumba ya zida zake
26 Mumenyane naye Babuloni mbali zonse.
27 Iphani ankhondo ake onse.
28 Tikumva anthu othawa nkhondo ochokera ku Babuloni
29 “Itanani anthu oponya mivi kudzathira nkhondo Babuloni.
30 Nʼchifukwa chake, anyamata ake adzaphedwa mʼmabwalo ake;
31 “Taona, ndikukuthira nkhondo, iwe wodzikuzawe,”
32 Wodzikuzawe udzapunthwa nʼkugwa
33 Yehova Wamphamvuzonse akuti,
34 Koma Mpulumutsi wawo ndi wamphamvu;
35 Yehova akuti,
36 Imfa yalunjika pa aneneri abodza
37 Imfa ilunjike pa akavalo ake ndi magaleta ake.
38 Chilala chilunjike pa madzi ake
39 “Nʼchifukwa chake nyama zakuthengo ndi afisi zidzakhala kumeneko
40 Monga momwe Mulungu anawonongera Sodomu ndi Gomora
41 “Taonani! Gulu lankhondo likubwera kuchokera kumpoto;
42 Atenga mauta ndi mikondo;
43 Mfumu ya ku Babuloni yamva za mbiri yawo,
44 Taonani, monga mkango wochokera ku nkhalango ya ku Yorodani
45 Nʼchifukwa chake imvani.
46 Akadzagwa Babuloni padzakhala mfuwu waukulu ndipo dziko lapansi lidzanjenjemera,