1 Yehova ananena izi:
2 Koma nthawi ikubwera,”
3 “Lirani, inu anthu a ku Hesiboni chifukwa wowononga uja wafika!
4 Chifukwa chiyani mukunyadira
5 Ndidzabweretsa zoopsa pa iwe
6 “Komabe pambuyo pake, ndidzabwezera kwawo Aamoni,”
7 Yehova Wamphamvuzonse ananena izi za Edomu:
8 Inu anthu a ku Dedani, thawani,
9 Kodi anthu othyola mphesa akanafika kwa inu
10 Koma ine ndazivula zidzukulu za Esau.
11 ‘Siyani ana anu amasiye; Ine ndidzawateteza.
12 Yehova akuti, “Ngati iwo amene sanali oyenera kulangidwa adzamwa chikho cha chiweruzo, ndiye muyesa kuti inuyo simudzalangidwa? Ayi ndithu simudzakhala osalangidwa. Mudzamwa ndithu chikhocho.
13 Ine ndikulumbira, akutero Yehova, kuti mzinda wa Bozira udzasanduka bwinja, chinthu chochititsa mantha, chomachiseka ndiponso chotembereredwa. Mizinda yake yonse idzakhala mabwinja mpaka muyaya.”
14 Ndamva uthenga wochokera kwa Yehova:
15 “Ndidzakuchepetsani pakati pa anthu a mitundu ina.
16 Kuopseza kwako kwakunyenga;
17 “Dziko la Edomu lidzasanduka chinthu chochititsa mantha.
18 Monga momwe anawonongekera Sodomu ndi Gomora,
19 “Monga mkango wotuluka ku nkhalango za ku Yorodani
20 Nʼchifukwa chake imvani. Izi ndi zimene Ine Yehova
21 Akadzagwa Edomu padzakhala mfuwu waukulu ndipo dziko lapansi lidzanjenjemera;
22 Taonani, mtundu wina udzachita kuwuluka
23 Mawu a Yehova onena za Damasiko ndi awa:
24 Anthu a ku Damasiko alefuka.
25 Mzinda wotchuka
26 Nʼchifukwa chake anyamata ake adzagwa mʼmisewu ndi kufa;
27 “Ndidzatentha malinga a Damasiko;
28 Mawu a Yehova onena za Kedara ndi maufumu a ku Hazori, amene Nebukadinezara mfumu ya Babuloni anawagonjetsa ndi awa:
29 Landani matenti awo ndi nkhosa zawo,
30 “Thawani mofulumira!
31 “Nyamukani kathireni nkhondo mtundu wa anthu umene uli pamtendere,
32 Ngamira zawo zidzafunkhidwa,
33 “Hazori adzasanduka bwinja,
34 Uthenga umene Yehova anapatsa mneneri Yeremiya wonena za Elamu, Zedekiya mfumu ya Yuda atangoyamba kulamulira ndi uwu:
35 Yehova Wamphamvuzonse akuti,
36 Ndidzabweretsa mphepo zinayi pa Elamu
37 A ku Elamuwo ndidzachititsa mantha pamaso pa adani awo
38 Ndidzakhazika mpando wanga waufumu ku Elamu
39 “Komabe mʼtsogolomo ndidzabwezera