1 Ponena za Mowabu:
2 Palibenso amene akutamanda Mowabu;
3 Tamvani mfuwu wa anthu a ku Horonaimu.
4 Mowabu wawonongeka;
5 Anthu akukwera chikweza cha ku Luhiti,
6 Thawani! Dzipulumutseni;
7 Popeza inu munkadalira ntchito zanu ndi chuma chanu,
8 Wowononga adzabwera ndi kusakaza mzinda uliwonse,
9 Mtsineni khutu Mowabu
10 “Wotembereredwa munthu amene amagwira ntchito ya Yehova monyinyirika!
11 “Mowabu wakhala pa mtendere kuyambira ubwana wake,
12 Nʼchifukwa chake masiku akubwera,”
13 Pamenepo Mowabu adzachita manyazi ndi Kemosi,
14 “Kodi munganene bwanji kuti, ‘Ife ndife asilikali.
15 Owononga Mowabu ndi mizinda yake abwera ndipo ankhondo adzalowa mʼmidzi yake;
16 Kugwa kwa Mowabu kuli pafupi;
17 Mulireni kwambiri, inu nonse amene mwamuzungulira,
18 “Tsikani pa ulemerero wanu
19 Inu amene mumakhala ku Aroeri,
20 Iwo adzayankha kuti, “Mowabu wachititsidwa manyazi, pakuti wasakazika.
21 Chiweruzo chabwera ku mizinda ya ku mapiri,
22 Diboni, Nebo, Beti-Dibilataimu,
23 Kiriyataimu, Beti-Gamuli, Beti-Meoni,
24 Keriyoti ndi Bozira
25 Mphamvu za Mowabu zawonongeka;
26 “Muledzeretseni Mowabu,
27 Kodi suja Israeli anali kwa iwe ngati chinthu chomachiseka?
28 Inu amene mumakhala ku Mowabu,
29 “Tamva za kunyada kwa Mowabu,
30 Ine ndikuzidziwa ntchito zake,
31 Nʼchifukwa chake ndidzamulira Mowabu,
32 Ndikukhetsa misozi chifukwa cha inu, kupambana momwe ndinalirira Yazeri.
33 Chimwemwe ndi chisangalalo zatha
34 “A ku Hesiboni ndi Eleali akulira
35 Ndidzawaletsa anthu a ku Mowabu
36 “Nʼchifukwa chake mtima wanga ukulirira Mowabu ngati chitoliro.
37 Aliyense wameta mutu wake
38 Pa madenga onse a ku Mowabu
39 “Taonani mmene waphwanyikira! Tamvani momwe akulirira!
40 Yehova akuti,
41 Mizinda idzagwidwa
42 Mowabu sudzakhala mtundu wa anthu
43 Zoopsa, dzenje ndi msampha zikudikira
44 “Aliyense wothawa zoopsa
45 “Anthu othawa nkhondo ayima pa mthunzi wa Hesiboni
46 Tsoka kwa iwe Mowabu!
47 “Komabe masiku akutsogolo