Jeremias 47

NYA

1 Uthenga umene Yehova anamupatsa mneneri Yeremiya wonena za Afilisti, Farao asanathire nkhondo Gaza ndi uwu:

2 Yehova akuti,

3 akadzamva mgugu wa ngʼombe zazimuna zothamanga,

4 Pakuti tsiku lafika

5 Anthu a ku Gaza ameta mipala;

6 “Mukulira kuti, ‘Aa, lupanga la Yehova,

7 Koma lupangalo lidzapumula bwanji

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado