1 Uthenga umene Yehova anamupatsa mneneri Yeremiya wonena za Afilisti, Farao asanathire nkhondo Gaza ndi uwu:
2 Yehova akuti,
3 akadzamva mgugu wa ngʼombe zazimuna zothamanga,
4 Pakuti tsiku lafika
5 Anthu a ku Gaza ameta mipala;
6 “Mukulira kuti, ‘Aa, lupanga la Yehova,
7 Koma lupangalo lidzapumula bwanji