1 Yehova anamupatsa Yeremiya uthenga wonena za anthu a mitundu ina.
2 Kunena za Igupto:
3 anati, “Konzani zishango zanu ndi malihawo,
4 Mangani akavalo,
5 Yeremiya anati: Kodi ndikuona chiyani?
6 Waliwiro sangathe kuthawa
7 “Kodi ndani amene akukwera ngati Nailo,
8 Igupto akusefukira ngati Nailo,
9 Tiyeni, inu akavalo!
10 Koma tsikulo ndi la Ambuye Yehova Wamphamvuzonse;
11 “Pita ku Giliyadi ukatenge mankhwala
12 Anthu a mitundu ina amva za manyazi ako;
13 Uthenga umene Yehova anapatsa mneneri Yeremiya wonena za kubwera kwa Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni kudzathira nkhondo Igupto ndi uwu:
14 “Mulengeze ku Igupto. Mulengeze ku Migidoli.
15 Chifukwa chiyani mulungu wanu wamphamvu uja Apisi wathawa?
16 Ankhondo anu apunthwa ndi kugwa.
17 Kumeneku iwo adzafuwula kuti,
18 “Pali Ine wamoyo,” ikutero Mfumu,
19 Konzani katundu wanu wopita naye ku ukapolo
20 “Igupto ali ngati mwana wangʼombe wokongola,
21 Ngakhale ankhondo aganyu amene ali naye
22 Aigupto akuthawa ndi liwu lawo lili ngati la njoka yothawa
23 Iwo adzadula nkhalango ya Igupto,”
24 Anthu a ku Igupto achita manyazi
25 Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli, akunena kuti, “Ndili pafupi kulanga Amoni mulungu wa Tebesi. Ndidzalanganso Farao ndi Igupto pamodzi ndi milungu yake yonse, mafumu ake ndi onse amene amamukhulupirira.
26 Ndidzawapereka kwa amene akufuna kuwapha, ndiye kuti kwa Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni ndi atsogoleri ake ankhondo. Komabe, mʼtsogolomo Igupto adzakhalanso ndi anthu monga kale,” akutero Yehova.
27 “Iwe mtumiki wanga Yakobo, usachite mantha;
28 Iwe mtumiki wanga Yakobo, usachite mantha,