1 “Pitani uku ndi uku mʼmisewu ya Yerusalemu,
2 Ngakhale anthu akulumbira kuti, ‘Pali Yehova wamoyo,’
3 Inu Yehova, kodi suja mumafuna anthu onena zoona?
4 Ndiye ndinati, “Awa ndi amphawi chabe;
5 Tsono ndidzapita kwa atsogoleri
6 Choncho mkango wochokera ku nkhalango udzawapha,
7 Yehova akuti, “Kodi ndingakukhululukireni bwanji ndi zimene mwachita?
8 Monga amachitira akavalo onenepa akamamemesa,
9 Tsono ndingaleke kuwalanga chifukwa cha zimenezi?”
10 “Pitani ku minda yake ya mipesa ndi kukayiwononga,
11 Nyumba ya Israeli ndi nyumba ya Yuda
12 Iwowa ankanama ponena za Yehova kuti,
13 Mawu a aneneri azidzangopita ngati mphepo;
14 Chifukwa chake Yehova Mulungu Wamphamvuzonse akuti,
15 Inu Aisraeli,” Yehova akuti,
16 Zida zawo za nkhondo zapha anthu ambirimbiri;
17 Adzakudyerani zokolola zanu ndi chakudya chanu,
18 “Komabe pa masiku amenewo sindidzakuwonongani kotheratu,” akutero Yehova.
19 Ndipo pamene anthu adzafunsa Yehova kuti, “Chifukwa chiyani Yehova Mulungu wathu wachita zimenezi?” Iwe udzawawuze kuti, “Monga momwe mwasiyira Ine ndi kutumikira milungu yachilendo mʼdziko mwanu, momwemonso mudzatumikira anthu a mʼdzikonso lachilendo.”
20 “Lengeza izi kwa ana a Yakobo
21 Imvani izi, inu anthu opusa ndi opanda nzeru,
22 Kodi simuyenera kuchita nane mantha?”
23 Koma anthu awa ndi nkhutukumve ndiponso a mitima yowukira;
24 Sananenepo mʼmitima mwawo kuti,
25 Koma zolakwa zanu zalepheretsa zonsezi;
26 “Pakati pa anthu anga pali anthu ena oyipa
27 Nyumba zawo zadzaza ndi chuma chochipeza mwa chinyengo
28 Ndipo ananenepa ndi kukhala ndi matupi osalala.
29 Kodi Ine ndingaleke kuwalanga chifukwa cha zimenezi?
30 “Chinthu chothetsa nzeru ndi choopsa kwambiri
31 Aneneri akunenera zabodza,