1 “Ngati mukufuna kubwerera, inu Aisraeli,
2 Muzilumbira mokhulupirika ndiponso mwa chilungamo
3 Zimene Yehova akunena kwa anthu a ku Yuda ndi a ku Yerusalemu ndi izi:
4 Dziperekeni nokha kwa Ine
5 “Lengeza ku Yuda ndi kulalikira mu Yerusalemu kuti,
6 Kwezani mbendera kuyangʼana ku Ziyoni!
7 Monga mkango umatulukira mʼngaka yake
8 Choncho valani ziguduli,
9 “Pa tsiku limenelo, mfumu ndi nduna zake adzataya mtima,
10 Ndipo ine ndinati, “Haa, Ambuye Yehova, ndithu munawanyenga anthu awa pamodzi ndi Yerusalemu pamene munanena kuti, ‘Mudzakhala pa mtendere,’ chonsecho lupanga lili pakhosi pathu.”
11 Nthawi imeneyo anthu awa ndi Yerusalemu adzawawuza kuti, “Mphepo yotentha yochokera ku magomo a mʼchipululu ikuwomba pa anthu anga, osati mphepo yopeta kapena yoyeretsa;
12 koma mphepo yamphamvu kwambiri yochokera kwa Ine. Tsono ndi Ineyo amene ndikuwaweruza.”
13 Taonani, adani akubwera ngati mitambo,
14 Iwe Yerusalemu, tsuka mtima wako kuchotsa zoyipa kuti upulumuke.
15 Pakuti amithenga akulalika mawu mʼdziko la Dani;
16 Iwo akuti, “Fotokozani zimenezi kwa anthu a mitundu ina,
17 Azinga Yerusalemu ngati anthu olondera munda,
18 “Makhalidwe anu ndi zochita zanu
19 Mayo, mayo,
20 Tsoka limatsata tsoka linzake;
21 Kodi ndikhale ndikuona mbendera ya nkhondo,
22 Yehova akuti, “Anthu anga ndi zitsiru;
23 Ndinayangʼana dziko lapansi,
24 Ndinayangʼana mapiri,
25 Ndinayangʼana, ndipo sindinaone anthu;
26 Ndinayangʼana, dziko lachonde linali litasanduka chipululu;
27 Yehova akuti,
28 Chifukwa chake dziko lapansi lidzalira
29 Pakumva phokoso la okwera pa akavalo ndi la anthu oponya mivi,
30 Iwe Yerusalemu, ndiwe bwinja!
31 Ndikumva kulira ngati kwa mayi pa nthawi yake yobereka,