Jeremias 6

NYA

1 “Thawani, inu anthu a ku Benjamini!

2 Kodi mzinda wa Ziyoni suli ngati msipu wokongola kwambiri,

3 Abusa ndi nkhosa zawo adzabwera kudzalimbana nawo;

4 Adzanena kuti, “Konzekani kuwuthira nkhondo mzindawo!

5 Tsono nyamukani kuti tiwuthire nkhondo mzindawu usiku uno

6 Yehova Wamphamvuzonse akuti,

7 Monga momwe chitsime chimatulutsira madzi

8 Iwe Yerusalemu, tengapo phunziro,

9 Yehova Wamphamvuzonse anandiwuza kuti,

10 Kodi ndiyankhule ndi yani ndi kumuchenjeza?

11 Koma ine ndadzazidwa ndi mkwiyo wa Yehova,

12 Nyumba zawo adzazipereka kwa ena,

13 “Kuyambira wamngʼono mpaka wamkulu,

14 Amapoletsa zilonda za anthu anga

15 Kodi amachita manyazi akamachita zonyansazo?

16 Yehova akuti,

17 Ine ndinakupatsani alonda oti akuyangʼanireni

18 Nʼchifukwa chake imvani, inu anthu a mitundu ina;

19 Imvani, inu anthu okhala pa dziko lapansi,

20 Kodi pali phindu lanji ngakhale mubwere ndi lubani kuchokera ku Seba,

21 Choncho Yehova akuti,

22 Yehova akunena kuti,

23 Atenga mauta ndi mikondo;

24 A ku Ziyoni akuti “Ife tamva mbiri yawo,

25 Musapite ku minda

26 Inu anthu anga, valani ziguduli

27 “Iwe Yeremiya, ndakuyika kuti ukhale choyesera zitsulo.

28 Onsewo ali ndi khalidwe lokanika ndi lowukira

29 Moto mu mvukuto ukuyaka kwambiri;

30 Iwo ali ngati siliva wotayidwa,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado