Jó 9

NYA

1 Ndipo Yobu anayankha kuti,

2 “Zoonadi, ndikudziwa kuti zimenezi ndi zoona.

3 Ngakhale wina atafuna kutsutsana naye,

4 Mulungu ndi wa nzeru zambiri ndipo mphamvu zake ndi zochuluka.

5 Iye amasuntha mapiri, mapiriwo osadziwa,

6 Iye amagwedeza dziko lapansi kulisuntha pamalo pake

7 Iye amayankhula ndi dzuwa ndipo siliwala;

8 Ndi Mulungu yekha amene anayala mayiko akumwamba

9 Iye ndiye mlengi wa nyenyezi zamlalangʼamba ndi akamwiniatsatana,

10 Iye amachita zozizwitsa zimene sizimvetsetseka,

11 Akapita pafupi ndi ine sindingathe kumuona;

12 Ngati Iye alanda zinthu, ndani angathe kumuletsa?

13 Mulungu sabweza mkwiyo wake;

14 “Nanga ine ndingathe kukangana naye bwanji?

15 Ngakhale nditakhala wosalakwa, sindingamuyankhe;

16 Ngakhale ndikanamuyitana ndipo Iye ndi kuvomera,

17 Iye akanandikantha ndi mphepo yamkuntho,

18 Mulungu sakanandilola kuti ndipumenso

19 Tikanena za mphamvu, Iye ndi wamphamvudi!

20 Ngakhale ndikanakhala wosalakwa, zoyankhula zanga zikananditsutsa;

21 “Ngakhale ine ndili wosalakwa,

22 Zonse nʼzofanana; nʼchifukwa chake ndikuti,

23 Pamene mkwapulo ubweretsa imfa yadzidzidzi,

24 Pamene dziko lagwa mʼmanja mwa anthu oyipa

25 “Masiku anga ndi othamanga kwambiri kupambana munthu waliwiro;

26 Amayenda ngati mabwato a njedza pa nyanja,

27 Nʼtanena kuti, ‘Ndidzayiwala madandawulo anga,

28 ndikuopabe mavuto anga onse,

29 Popeza ndapezeka kale wolakwa

30 Ngakhale nditasamba mʼmadzi oyera kwambiri

31 mutha kundiponyabe pa dzala,

32 “Mulungu si munthu ngati ine kuti ndithe kumuyankha,

33 Pakanapezeka munthu wina kuti akhale mʼkhalapakati wathu,

34 munthu wina woti achotse ndodo ya Mulungu pa ine

35 Pamenepo ine ndikanatha kuyankhula mosamuopa Mulunguyo,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado