Jó 8

NYA

1 Pamenepo Bilidadi wa ku Suki anayankha kuti,

2 “Kodi udzakhala ukuyankhula zoterezi mpaka liti?

3 Kodi Mulungu amapotoza chiweruzo cholungama?

4 Pamene ana ako anamuchimwira Mulungu,

5 Koma utayangʼana kwa Mulungu,

6 ngati uli wangwiro ndi wolungama mtima

7 Chiyambi chako chidzaoneka ngati chochepa

8 “Funsa kwa anthu amvulazakale

9 pakuti ife ndife ana adzulodzuloli ndipo sitidziwa chilichonse,

10 Kodi iwo sadzakulangiza ndi kukufotokozera?

11 Kodi bango nʼkumera pa nthaka yopanda chinyontho?

12 Popanda madzi, zimenezi zimafota zikanali zaziwisi ndi zosadula;

13 Ndimo mmene amachitira anthu onse amene amayiwala Mulungu;

14 Kulimba mtima kwake kumafowoka;

15 Iye amatsamira ukonde wake, koma umaduka;

16 Munthu woyipayo ali ngati chomera chothiriridwa bwino chimene chili pa dzuwa,

17 mizu yake imayanga pa mulu wa miyala

18 Koma pamene yachotsedwa pamalo pakepo,

19 Ndithudi chomeracho chimafota,

20 “Ndithudi, Mulungu sakana munthu amene alibe cholakwa

21 Iye adzadzaza mʼkamwa mwako ndi phwete

22 Adani ako adzachita manyazi,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado