Jó 7

NYA

1 “Kodi munthu sakhala ndi ntchito yowawa pa dziko lapansi?

2 Monga ngati kapolo wolakalaka mthunzi wa nthawi yamadzulo,

3 choncho ine ndapatsidwa nthawi yongovutika pachabe,

4 Ndikamagona ndimaganiza kuti, ‘Kodi kucha liti?’

5 Thupi langa ladzala mphutsi ndi zipsera,

6 “Masiku anga ndi othamanga kupambana makina wolukira nsalu,

7 Inu Mulungu kumbukirani kuti moyo wanga uli ngati mpweya;

8 Amene akundiona tsopano akundiona;

9 Monga mtambo umazimirira ndi kukanganuka,

10 Iye sadzabweranso ku nyumba kwake

11 “Nʼchifukwa chake ine sindidzakhala chete;

12 Kodi ine ndine nyanja kapena chirombo chamʼnyanja

13 Pamene ndikuganiza kuti ndidzapeza chitonthozo pa bedi panga

14 ngakhale nthawi imeneyo mumandiopseza ndi maloto

15 kotero kuti ndimalakalaka kudzikhweza kapena kufa,

16 Ine ndatopa nawo moyo wanga; sindingakonde kukhala moyo nthawi zonse.

17 “Kodi munthu nʼchiyani kuti muzimuganizira chotere,

18 kuti muzimusanthula mmawa uliwonse

19 Kodi simudzaleka kumandizonda

20 Ngati ine ndachimwa, ndachita chiyani kwa Inu,

21 Chifukwa chiyani simukundikhululukira zolakwa zanga

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado