Jó 10

NYA

1 “Ine ndatopa nawo moyo wanga;

2 Ndidzati kwa Mulungu wanga: Musandiweruze kuti ndine wolakwa,

3 Kodi mumakondwera mukamandizunza,

4 Kodi maso anu ali ngati a munthu?

5 Kodi masiku anu ali ngati masiku a munthu,

6 kuti Inu mufufuze zolakwa zanga

7 ngakhale mukudziwa kuti sindine wolakwa

8 “Munandiwumba ndi kundipanga ndi manja anu.

9 Kumbukirani kuti munandipanga ndi dothi,

10 Suja munapatsa abambo anga mphamvu zoti andibale,

11 Munandikuta ndi khungu ndi mnofu

12 Munandipatsa moyo ndi kundionetsa chifundo chanu,

13 “Koma izi ndi zimene munabisa mu mtima mwanu,

14 Kuti ngati ndingachimwe mudzakhala mukundipenyetsetsa

15 Ngati ndili wolakwa, tsoka langa!

16 Ndipo ndikatukula mutu wanga, Inu mumandisaka ngati mkango

17 Mumabweretsa mboni zatsopano potsutsana nane

18 “Chifukwa chiyani Inu munalola kuti ndibadwe?

19 Ndikanapanda kubadwa,

20 Kodi masiku anga owerengeka sali pafupi kutha?

21 ndisanapite ku malo amene munthu sabwererako

22 ku dziko la mdima wandiweyani

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado