Jó 11

NYA

1 Pamenepo Zofari wa ku Naama anayankha kuti,

2 “Kodi mawu ambirimbiriwa nʼkukhala osayankhidwa?

3 Kodi anthu nʼkukhala chete atamva kubwebweta kwakoku?

4 Iwe ukunena kwa Mulungu kuti, ‘Zikhulupiriro zanga ndi zopanda zolakwika

5 Aa, nʼkanakonda Mulungu akanayankhula

6 ndi kukuwululira chinsinsi cha nzeru yake,

7 “Kodi iwe ungathe kumvetsa zinsinsi za Mulungu?

8 Zili kutali kupambana mayiko akumwamba, nanga ungachite chiyani?

9 Muyeso wa nzeru zake ndi wautali kupambana dziko lapansi

10 “Ngati Iye atabwera ndi kukutsekera mʼndende

11 Ndithudi, Mulungu amazindikira anthu achinyengo;

12 Munthu wopanda nzeru sizingatheke kukhala wanzeru

13 “Koma ngati upereka mtima wako kwa Iye

14 ngati utaya tchimo limene lili mʼdzanja lako

15 udzatukula mutu wako wosachita manyazi;

16 Udzayiwala ndithu zowawa zako,

17 Moyo wako udzawala kupambana usana,

18 Udzalimba mtima popeza pali chiyembekezo;

19 Udzagona pansi, popanda wina wokuopseza

20 Koma anthu oyipa adzafuna thandizo osalipeza,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado