1 Pamenepo Yobu anayankha kuti,
2 “Ndithudi inuyo ndinu anthu
3 Koma inenso ndili nazo nzeru ngati inu;
4 “Ndasanduka chinthu choseketsa kwa abwenzi anga,
5 Anthu amene ali pabwino amanyoza anzawo amene ali pa tsoka.
6 Nyumba za anthu achifwamba zimakhala pa mtendere,
7 “Koma funsa nyama zakuthengo ndipo zidzakuphunzitsa,
8 kapena uyankhule ndi dziko lapansi ndipo lidzakuphunzitsa,
9 Kodi mwa zonsezi ndi chiti chimene sichidziwa
10 Mʼmanja mwake ndi mʼmene muli moyo wa cholengedwa chilichonse,
11 Kodi khutu sindiye limene limamva mawu
12 Kodi nzeru sipezeka pakati pa anthu okalamba?
13 “Kwa Mulungu ndiye kuli nzeru ndi mphamvu;
14 Chimene Iye wapasula palibe angachimangenso.
15 Iyeyo akamanga mvula dziko limawuma;
16 Kwa Iye kuli mphamvu ndi kupambana;
17 Iye amalanda aphungu nzeru zawo
18 Iye amachotsa zingwe zimene mafumu anawamanga nazo
19 Iye amasocheretsa ansembe atawalanda nzeru zawo
20 Iye amakhalitsa chete aphungu odalirika
21 Iye amanyoza anthu otchuka
22 Iye amatulutsira poyera zinthu zozama za mu mdima
23 Iye amakuza mitundu ya anthu ndipo amayiwononganso;
24 Iye amalanda nzeru za atsogoleri a dziko lapansi;
25 Iwo amafufuzafufuza njira mu mdima wopanda chowunikira;