Jó 12

NYA

1 Pamenepo Yobu anayankha kuti,

2 “Ndithudi inuyo ndinu anthu

3 Koma inenso ndili nazo nzeru ngati inu;

4 “Ndasanduka chinthu choseketsa kwa abwenzi anga,

5 Anthu amene ali pabwino amanyoza anzawo amene ali pa tsoka.

6 Nyumba za anthu achifwamba zimakhala pa mtendere,

7 “Koma funsa nyama zakuthengo ndipo zidzakuphunzitsa,

8 kapena uyankhule ndi dziko lapansi ndipo lidzakuphunzitsa,

9 Kodi mwa zonsezi ndi chiti chimene sichidziwa

10 Mʼmanja mwake ndi mʼmene muli moyo wa cholengedwa chilichonse,

11 Kodi khutu sindiye limene limamva mawu

12 Kodi nzeru sipezeka pakati pa anthu okalamba?

13 “Kwa Mulungu ndiye kuli nzeru ndi mphamvu;

14 Chimene Iye wapasula palibe angachimangenso.

15 Iyeyo akamanga mvula dziko limawuma;

16 Kwa Iye kuli mphamvu ndi kupambana;

17 Iye amalanda aphungu nzeru zawo

18 Iye amachotsa zingwe zimene mafumu anawamanga nazo

19 Iye amasocheretsa ansembe atawalanda nzeru zawo

20 Iye amakhalitsa chete aphungu odalirika

21 Iye amanyoza anthu otchuka

22 Iye amatulutsira poyera zinthu zozama za mu mdima

23 Iye amakuza mitundu ya anthu ndipo amayiwononganso;

24 Iye amalanda nzeru za atsogoleri a dziko lapansi;

25 Iwo amafufuzafufuza njira mu mdima wopanda chowunikira;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado