Jó 40

NYA

1 Yehova anati kwa Yobu:

2 “Kodi iwe ufuna kukangana ndi Wamphamvuzonse?

3 Pamenepo Yobu anayankha Yehova:

4 “Ine sindili kanthu konse,

5 Ndinayankhula kamodzi, koma pano ndilibe yankho,

6 Ndipo Yehova anayankha Yobu mʼkamvuluvulu kuti,

7 “Tsopano vala dzilimbe ngati mwamuna;

8 “Kodi iwe unganyoze chiweruzo changa cholungama?

9 Kodi uli ndi dzanja monga la Mulungu,

10 Ngati zili choncho udzikometsere ndi ulemerero ndi kukongola,

11 Tsanula ukali wako wosefukirawo,

12 Uyangʼane aliyense wodzikweza ndipo umutsitse,

13 Onsewo uwakwirire pamodzi mfumbi;

14 Ukatero Ine ndidzakuvomereza

15 “Taganiza za mvuwu,

16 Mphamvu zake ndi zazikulu kwambiri,

17 Mchira wake umayima tolotolo ngati mtengo wamkungudza;

18 Mafupa ake ali ngati mapayipi amkuwa,

19 Mvuwuyo ndi yayikulu mwa zolengedwa za Mulungu,

20 Imapeza chakudya chake ku mtunda

21 Imagona pa tsinde pa zitsamba za mipeta,

22 Imaphimbika ndi mthunzi wazitsamba za mipeta;

23 Madzi a mu mtsinje akakokoma, sichita mantha,

24 Kodi alipo amene angathe kukola mvuwu ndi mbedza

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado