1 “Kodi ungathe kukoka ngʼona ndi mbedza ya nsomba
2 Kodi ungathe kumanga chingwe mʼmphuno mwake,
3 Kodi ngʼonayo idzakupempha kuti uyichitire chifundo?
4 Kodi idzachita nawe mgwirizano
5 Kodi udzasewera nayo ngati mbalame,
6 Kodi anthu adzayitsatsa malonda?
7 Kodi chikopa chake ungathe kuchilasa ndi zisonga,
8 Ukayiputa udziwe kuti pali nkhondo,
9 Chiyembekezo choti nʼkuyigonjetsa ndi chabodza;
10 Palibe wolimba mtima kuti ndi kuyiputa.
11 Kodi ndani anandipatsa kanthu kuti ndimubwezere?
12 “Sindidzaleka kuyankhula za ziwalo zake za chirombocho,
13 Ndani angasende chikopa chake?
14 Ndani angatsekule kukamwa kwake,
15 Kumsana kwake kuli mizere ya mamba
16 Mambawo ndi olukanalukana
17 Ndi olumikizanalumikizana;
18 Kuyetsemula kwake kumatulutsa mbaliwali;
19 Mʼkamwa mwake mumatuluka nsakali zamoto ndipo
20 Mʼmphuno mwake mumatuluka utsi
21 Mpweya wake umayatsa makala,
22 Mphamvu zake zili mʼkhosi mwake;
23 Minyewa ya thupi lake ndi yolumikizana ndipo
24 Pachifuwa pake ndi powuma ngati mwala,
25 Ngʼonayo ikangovuwuka,
26 Ngakhale ikanthidwe ndi lupanga, lupangalo silichita kanthu,
27 Chitsulo imachiyesa ngati phesi chabe
28 Muvi sungathe kuyithawitsa,
29 Zibonga zimakhala ngati ziputu;
30 Mamba a ku mimba kwake ali ngati chopunthira chakunthwa ndipo
31 Imagadutsa madzi ozama ngati madzi a mʼnkhali,
32 Kumbuyo kwake imasiya nthubwitubwi zambee,
33 Pa dziko lapansi palibe china chofanana nacho,
34 Chimanyoza nyama zina zonse;