Jó 4

NYA

1 Pamenepo Elifazi wa ku Temani anayankha kuti,

2 “Ngati wina atakuyankha, kodi ungakhumudwe?

3 Taganiza momwe iwe walangizira anthu ambiri,

4 Mawu ako analimbitsa anthu ofuna kugwa;

5 Koma tsopano mavuto akufikira ndipo wataya mtima,

6 Kodi kuopa Mulungu kwako sindiko kulimbika mtima kwako?

7 “Ganiza bwino tsopano: Kodi munthu wosalakwa anawonongekapo nʼkale lonse?

8 Monga ndaonera ine, anthu amene amatipula zoyipa,

9 Iwo amaphedwa ndi mpweya wa Mulungu;

10 Mikango imabangula ndi kulira,

11 Mkango umafa chifukwa chosowa nyama,

12 “Mawu anabwera kwa ine mwamseri,

13 Mʼkati mwa maloto ochititsa mantha usiku,

14 ndinagwidwa ndi mantha, ndi kuyamba kunjenjemera

15 Pamenepo mzimu unadutsa pamaso panga,

16 Chinthucho chinayimirira

17 ‘Kodi munthu angathe kukhala wolungama kupambana Mulungu?

18 Ngati Mulungu sakhulupirira atumiki ake omwe,

19 nanga kuli bwanji ndi iwo amene amakhala mʼnyumba zadothi,

20 Mmawa ali moyo, pofika madzulo afa;

21 Kodi zonse zimene ali nazo sizimatheratu,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado