Jó 37

NYA

1 “Mtima wanga ukulumphalumpha pa chimenechinso

2 Tamverani! Tamverani kubangula kwa liwu lake,

3 Iye amaponya chingʼaningʼani chake pansi pa thambo lonse

4 Pambuyo pake kubangula kwake kumamveka.

5 Liwu la Mulungu limabangula mʼnjira zambiri zodabwitsa

6 Amalamula chisanu chowundana kuti, ‘Igwa pa dziko lapansi,’

7 Kuti anthu onse amene anawalenga athe kuzindikira ntchito yake.

8 Zirombo zimakabisala

9 Mphepo yamkuntho imatuluka ku malo ake,

10 Mpweya wa Mulungu umawunditsa madzi

11 Iye amadzaza mitambo ndi madzi a mvula,

12 Mulungu amayendetsa mitamboyo

13 Iye amagwetsa mvula kuti alange anthu,

14 “Abambo Yobu, tamvani izi;

15 Kodi mukudziwa momwe Mulungu amayendetsera mitambo

16 Kodi mukudziwa momwe Mulungu amayalira mitambo,

17 Inu amene mʼzovala zanu mumatuluka thukuta

18 kodi mungathe kuthandizana naye kutambasula thambo

19 “Tiwuzeni ife zoti tikanene kwa Iye;

20 Kodi nʼkofunika kumudziwitsa Mulungu kuti ndili naye mawu?

21 Tsopano munthu sangathe kuyangʼana dzuwa,

22 Kuwala kwake kumaonekera cha kumpoto;

23 Wamphamvuzonse sitingathe kumufikira pafupi ndi wa mphamvu zoposa;

24 Nʼchifukwa chake anthu amamuopa kwambiri,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado