1 Ndipo Elihu anawonjeza kunena kuti,
2 “Kodi mukuganiza kuti mukukhoza?
3 Komanso inu mukufunsa kuti, ‘Kodi phindu langa nʼchiyani,
4 “Ine ndikufuna ndikuyankheni inu
5 Yangʼanani kumwamba ndipo muone
6 Inuyo mukachimwa, Iye zimamukhudza motani?
7 Ngati inu ndinu wolungama, mumamupatsa Iyeyo chiyani?
8 Kuyipa kwanu kumangokhudza anthu ngati inuyo,
9 “Anthu akufuwula chifukwa cha kuzunzidwa;
10 Koma palibe amene akunena kuti, ‘Kodi ali kuti Mulungu, Mlengi wanga,
11 amene amatiphunzitsa kupambana nyama za dziko lapansi
12 Iye sayankha pamene anthu akufuwulira kwa Iye
13 Ndithu, Mulungu samva kupempha kwawo kopanda pake;
14 Ndipo ndi bodza lalikulu kunena kuti
15 ndiye tsono popeza kuti ukali wake sukupereka chilango,
16 abambo Yobu mumangoyankhula zopandapake,