Jó 35

NYA

1 Ndipo Elihu anawonjeza kunena kuti,

2 “Kodi mukuganiza kuti mukukhoza?

3 Komanso inu mukufunsa kuti, ‘Kodi phindu langa nʼchiyani,

4 “Ine ndikufuna ndikuyankheni inu

5 Yangʼanani kumwamba ndipo muone

6 Inuyo mukachimwa, Iye zimamukhudza motani?

7 Ngati inu ndinu wolungama, mumamupatsa Iyeyo chiyani?

8 Kuyipa kwanu kumangokhudza anthu ngati inuyo,

9 “Anthu akufuwula chifukwa cha kuzunzidwa;

10 Koma palibe amene akunena kuti, ‘Kodi ali kuti Mulungu, Mlengi wanga,

11 amene amatiphunzitsa kupambana nyama za dziko lapansi

12 Iye sayankha pamene anthu akufuwulira kwa Iye

13 Ndithu, Mulungu samva kupempha kwawo kopanda pake;

14 Ndipo ndi bodza lalikulu kunena kuti

15 ndiye tsono popeza kuti ukali wake sukupereka chilango,

16 abambo Yobu mumangoyankhula zopandapake,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado