1 Tsono anthu atatuwa analeka kumuyankha Yobu, chifukwa chakuti iyeyo ankadziona kuti ndi wolungama.
2 Koma Elihu, mwana wa Barakeli, wa fuko la Buzi, wa banja la Ramu, anapsera mtima kwambiri Yobu chifukwa choti Yobuyo anakana kuvomera kuti anachimwa ndi kuti Mulungu anakhoza pomulanga.
3 Anapseranso mtima abwenzi ake atatu aja chifukwa sanapeze njira yomutsutsira Yobu, ngakhale iwo anamupeza kuti anali wolakwa.
4 Tsono Elihu anadikira kuti ayankhule ndi Yobu chifukwa choti abwenziwo anali akuluakulu kupambana iyeyo.
5 Koma Elihu ataona kuti anthu atatuwo analibe mawu oti ayankhulenso, iye anapsa mtima.
6 Choncho Elihu mwana wa Barakeli wa fuko la Buzi anati:
7 Ndimaganiza kuti, ‘Ayambe ndi akuluakulu kuyankhula;
8 Koma mzimu wa Mulungu mwa munthu,
9 Si okalamba amene ali ndi nzeru,
10 “Nʼchifukwa chake ndikuti, ‘Mvereni;
11 Ndadikira nthawi yonseyi,
12 ineyo ndinakumvetseranidi.
13 Musanene kuti, ‘Ife tapeza nzeru;
14 Koma Yobu sanayankhule motsutsana ndi ine,
15 “Iwo asokonezeka ndipo alibe choti ayankhulenso;
16 Kodi ine ndidikire chifukwa iwo sakuyankhula tsopano,
17 Inenso ndiyankhulapo tsopano;
18 Pakuti ndili nawo mawu ambiri,
19 mʼkati mwanga ndili ngati botolo lodzaza ndi vinyo,
20 Ndiyenera kuyankhula kuti mtima utsike;
21 Sindidzakondera munthu wina aliyense,
22 pakuti ndikanakhala wa luso loyankhula moshashalika,