Jó 31

NYA

1 “Ndinachita pangano ndi maso anga

2 Kodi Mulungu kumwambako wandisungira zotani?

3 Kodi si chiwonongeko kwa anthu oyipa,

4 Kodi Mulungu saona zochita zanga,

5 “Ngati ndachita zinthu mwachiphamaso,

6 Mulungu andiyeze ndi muyeso wake wolungama

7 ngati mayendedwe anga asempha njira,

8 Pamenepo ena adye zimene ndinadzala,

9 “Ngati mtima wanga unakopekapo ndi mkazi,

10 pamenepo mkazi wanga aphikire mwamuna wina chakudya,

11 Pakuti zimenezo zikanakhala zochititsa manyazi,

12 Ndi moto umene umayaka mpaka chiwonongeko;

13 “Ngati ndinkapondereza mlandu wa akapolo anga aamuna kapena aakazi,

14 ndidzatani pamene Mulungu adzanditsutsa?

15 Kodi amene anapanga ine mʼmimba mwa amayi anga si yemwe anapanganso iwo?

16 “Ngati ndinawamana aumphawi zinthu zimene ankazikhumba,

17 ngati chakudya changa ndinadya ndekha,

18 chonsechotu kuyambira unyamata wanga ndinamulera monga abambo ake,

19 ngati ndinaona wina aliyense akuzunzika ndi usiwa,

20 ndipo ngati iyeyo sananditamandepo

21 ngati ndinaopsezapo mwana wamasiye,

22 pamenepo phewa langa lipokonyeke,

23 Popeza ine ndinaopa kwambiri chiwonongeko chochokera kwa Mulungu,

24 “Ngati ndinayika mtima wanga pa chuma

25 ngati ndinakondwera chifukwa choti chuma changa chinali chambiri,

26 ngati pamene ndinaona dzuwa likuwala,

27 ndipo kuti mtima wanga unakopeka nazo

28 pamenepo zimenezinso zikanakhala machimo oti ndilangidwe nawo,

29 “Ngati ndinasangalala ndi kuwonongeka kwa mdani wanga,

30 ine sindinachimwe ndi pakamwa panga

31 ngati anthu amene ndimakhala nawo mʼnyumba mwanga sananenepo kuti,

32 Komatu mlendo sindinamusiye pa msewu usiku wonse,

33 ngati ndinabisa tchimo langa monga amachitira anthu ena,

34 chifukwa choopa gulu la anthu,

35 “Aa, pakanakhala wina wondimva!

36 Ndithu ine ndikanakoleka kalatayo pa phewa langa,

37 Ndikanamufotokozera zonse zimene ndinachita;

38 “Ngati minda yanga ikulira monditsutsa ine

39 ngati ndinadya za mʼminda mwake osapereka ndalama

40 pamenepo mʼmindamo mumere namsongole mʼmalo mwa tirigu

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado