1 Pali mgodi wa siliva
2 Chitsulo amachikumba pansi,
3 Munthu amalowa mu mdima atatenga nyale,
4 Amakumba njira zapansi mu mgodimo, kutali ndi kumene kumakhala anthu,
5 Nthaka, imene imatulutsa zakudya,
6 miyala ya safiro imachokera mʼmatanthwe ake,
7 Palibe mbalame yodya zinzake imene imadziwa njira yobisikayi,
8 Zirombo zolusa sizipondamo mʼnjiramo,
9 Munthu amaphwanya matanthwe olimba,
10 Amabowola njira mʼmatanthwewo;
11 Amaletsa mitsinje ya pansipo kuti isayendenso,
12 “Koma nzeru zingapezeke kuti?
13 Munthu sadziwa kufunika kwake kwa nzeruzo;
14 Phompho likuti, ‘Sizipezeka mwa ine muno.’
15 Nzeru sungazigule ndi golide wabwino kwambiri,
16 Nzeru singagulidwe ndi golide wa ku Ofiri,
17 Nzeru sungayiyerekeze ndi golide kapena mwala wa galasi,
18 Miyala ya korali ndi krisitali siyoyeneranso ndi kuyitchula nʼkomwe;
19 Nzeru sungayiyerekeze ndi miyala ya topazi ya ku Kusi;
20 “Kodi tsono nzeru zimachokera kuti?
21 Malo ake ndi obisika kwa zamoyo zonse,
22 Chiwonongeko ndi imfa zikuti,
23 Mulungu yekha ndiye amadziwa njira yake yopita kumeneko,
24 pakuti Iye amayangʼana mpaka ku malekezero a dziko lapansi
25 Iye atapatsa mphepo mphamvu zake,
26 atakhazikitsa lamulo loti mvula izigwa
27 pamenepo ndi pamene anayangʼana nzeruzo naziyeza mtengo wake;
28 Ndipo Iye anati kwa munthu,