Jó 27

NYA

1 Ndipo Yobu anapitiriza kuyankhula kwake:

2 “Ndithu pali Mulungu wamoyo, amene wakana kundiweruza molungama,

3 nthawi zonse pamene ndili ndi moyo,

4 pakamwa panga sipadzatuluka mawu oyipa,

5 Sindidzavomereza kuti inu mukunena zoona;

6 Ndidzasunga chilungamo changa ndipo sindidzalola kuti chindichokere;

7 “Mdani wanga akhale ngati woyipa,

8 Nanga chiyembekezo cha munthu wosapembedza nʼchiyani pamene aphedwa,

9 Kodi Mulungu amamva kulira kwake

10 Kodi adzapeza chikondwerero mwa Wamphamvuzonse?

11 “Ndidzakuphunzitsani za mphamvu ya Mulungu ndipo

12 Inu mwadzionera nokha zonsezi.

13 “Pano pali chilango chimene Mulungu amasungira woyipa,

14 Angakhale ana ake achuluke chotani adzaphedwa ndi lupanga ndipo

15 Amene adzatsalireko adzafa ndi mliri,

16 Ngakhale aunjike siliva ngati fumbi,

17 zimene wasungazo wolungama ndiye adzavale,

18 Nyumba imene akuyimanga ili ngati mokhala kadziwotche,

19 Amapita kokagona ali wolemera koma kutha kwake nʼkomweko;

20 Zoopsa zimamukokolola ngati madzi achigumula;

21 Mphepo ya kummawa imamuwulutsa ndipo iye saonekanso ndipo

22 Imakuntha pa iye osamuchitira chisoni,

23 Mphepoyo imamuwomba ndithu

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado