Jó 26

NYA

1 Pamenepo Yobu anayankha kuti,

2 “Wamuthandizadi munthu wopanda mphamvu!

3 Wapereka malangizo kwa munthu amene alibe nzeru!

4 Kodi wakuthandiza ndani kuti uyankhule mawu awa?

5 “Mizimu ya anthu akufa ikunjenjemera pansi pa madzi,

6 Dziko la anthu akufa ndi lapululu pamaso pa Mulungu;

7 Mulungu anayala thambo la kumpoto pa phompho;

8 Amasunga madzi ambiri mʼmitambo yake,

9 Iye amaphimba mwezi wowala,

10 Mulungu anawalembera madzi malire wonga uta,

11 Mizati yochirikiza mitambo yakumwamba imanjenjemera,

12 Ndi mphamvu zake anatontholetsa nyanja;

13 Ndi mpweya wake anayeretsa zamumlengalenga,

14 Zimenezi ndi pangʼono chabe mwa ntchito yake;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado