1 Apo Bilidadi wa ku Suki anayankha kuti,
2 “Ulamuliro ndi kuopsa ndi za Mulungu,
3 Kodi magulu ake ankhondo nʼkuwerengeka?
4 Kodi munthu angakhale bwanji wolungama pamaso pa Mulungu?
5 Ngati mwezi sutha kuwala kwenikweni,
6 nanji tsono munthu amene ali ngati mphutsi,