Jó 25

NYA

1 Apo Bilidadi wa ku Suki anayankha kuti,

2 “Ulamuliro ndi kuopsa ndi za Mulungu,

3 Kodi magulu ake ankhondo nʼkuwerengeka?

4 Kodi munthu angakhale bwanji wolungama pamaso pa Mulungu?

5 Ngati mwezi sutha kuwala kwenikweni,

6 nanji tsono munthu amene ali ngati mphutsi,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado