1 “Chifukwa chiyani Wamphamvuzonse sayikiratu nthawi yoti aweruze?
2 Anthu amasuntha miyala ya mʼmalire, kuti akuze dziko lawo;
3 Amalanda abulu a ana amasiye
4 Amachotsa mʼmisewu anthu osauka,
5 Amphawiwo amakhala ngati mbidzi mʼchipululu,
6 Iwo amakolola za mʼminda ya eni ake,
7 Amagona maliseche usiku wonse kusowa zovala;
8 Amavumbwa ndi mvula ya mʼmapiri
9 Amatsomphola mwana wamasiye wa ku bere;
10 Amphawi amangoyenda maliseche kusowa zovala;
11 Iwo amayenga mafuta a olivi mʼminda ya anthu oyipa;
12 Kubuwula kwa anthu amene akufa kumamveka kuchokera mu mzinda,
13 “Pali ena amene amakana kuwala,
14 Dzuwa likalowa, wopha anzake amadzuka
15 Munthu wachigololo amadikira chisisira;
16 Mbala zimathyola nyumba usiku,
17 Pakuti kwa onsewa mdima wandiweyani ndiye kuti kwawachera.
18 “Komatu iwowo ndi thovu loyandama pa madzi;
19 Monga momwe kutentha ndi chilala zimasungunulira madzi owundana
20 Mayi wowabereka amawayiwala,
21 Amachitira nkhanza mayi wosabala ndi mayi amene alibe mwana,
22 Koma Mulungu amawononga munthu wamphamvu mwa mphamvu zake;
23 Mulungu atha kuwalola kuti akhale mosatekeseka,
24 Kwa kanthawi kochepa oyipa amakwezedwa ndipo kenaka saonekanso;
25 “Ngati zimenezi sizoona, ndani angaonetse kuti ndine wabodza