Jó 23

NYA

1 Pamenepo Yobu anayankha kuti,

2 “Leronso kudandaula kwanga nʼkwakukulu kwambiri;

3 Ndikanangodziwa kumene ndikanamupeza Mulungu;

4 Ndikanafotokoza mlandu wanga pamaso pake

5 Ndikanadziwa mawu amene Iye akanandiyankha,

6 Kodi Iye akanalimbana nane mwa mphamvu zake zazikulu?

7 Kumeneko munthu wolungama akanafotokoza mlandu wake pamaso pake,

8 “Taonani, ndikapita kummawa, Iye kulibe kumeneko,

9 Akamagwira ntchito kumpoto, sindimuona kumeneko

10 Koma Iye amadziwa mmene ndimayendera;

11 Mapazi anga akhala akuponda mʼmapazi ake;

12 Sindinapatuke kusiya malamulo ochokera pakamwa pake;

13 “Koma Iyeyo ndi wosasinthika, ndipo ndani angatsutsane naye?

14 Iye amachita chimene watsimikiza kuti chindichitikire,

15 Nʼchifukwa chake ndikuchita mantha kwambiri pamaso pake;

16 Mulungu walefula mtima wanga;

17 Komatu sindinachititsidwe mantha ndi mdima,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado