Jó 21

NYA

1 Pamenepo Yobu anayankha kuti,

2 “Mvetserani bwino mawu anga;

3 Ndiloleni ndiyankhule

4 “Kodi ine ndikudandaulira munthu?

5 Ndipenyeni ndipo mudabwe;

6 Ndikamaganiza zimenezi ndimachita mantha kwambiri;

7 Chifukwa chiyani anthu oyipa amakhalabe ndi moyo,

8 Amaona ana awo akukhazikika pamodzi nawo,

9 Mabanja awo amakhala pa mtendere ndipo sakhala ndi mantha;

10 Ngʼombe zawo zazimuna sizilephera kubereketsa;

11 Amatulutsa ana awo ngati gulu la nkhosa;

12 Amayimba nyimbo pogwiritsa ntchito matambolini ndi azeze;

13 Zaka zawo zimatha ali mu ulemerero

14 Koma anthuwo amawuza Mulungu kuti, ‘Tichokereni!’

15 Kodi Wamphamvuzonseyo ndani kuti timutumikire?

16 Komatu ulemerero wawo suli mʼmanja mwawo,

17 “Koma nʼkangati kamene nyale ya anthu oyipa imazimitsidwa?

18 Nʼkangati kamene iwo amakhala ngati phesi lowuluka ndi mphepo,

19 Paja amati, ‘Mulungu amalanga ana chifukwa cha machimo abambo awo.’

20 Mulole kuti adzionere yekha chilango chake,

21 Nanga kodi amalabadira chiyani zabanja lake limene walisiya mʼmbuyo,

22 “Kodi alipo wina amene angaphunzitse Mulungu nzeru,

23 Munthu wina amamwalira ali ndi mphamvu zonse,

24 thupi lake lili lonenepa,

25 Munthu wina amamwalira ali wowawidwa mtima,

26 Olemera ndi osauka omwe amamwalira ndi kuyikidwa mʼmanda

27 “Ndikudziwa bwino zimene mukuganiza,

28 Inu mukuti, ‘Kodi nyumba ya mkulu uja ili kuti,

29 Kodi munawafunsapo anthu amene ali pa ulendo?

30 Zakuti munthu woyipa amasungidwa chifukwa cha tsiku la tsoka,

31 Kodi ndani amadzudzula munthu wochimwayo?

32 Iye amanyamulidwa kupita ku manda

33 Dothi la ku chigwa limamukomera;

34 “Nanga inu mudzanditonthoza bwanji ine ndi mawu anu opandapakewo

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado