Jó 20

NYA

1 Pamenepo Zofari wa ku Naama anayankha kuti

2 “Kuvutika kwa mʼmaganizo kwanga kwandifulumiza kuti ndiyankhe

3 Ndikumva kudzudzula kondinyoza,

4 “Ndithudi iwe ukudziwa momwe zinthu zakhala zikuchitikira kuyambira kale,

5 kuti chisangalalo cha woyipa nʼchosachedwa kutha,

6 Ngakhale atamayenda mapewa ake ali mmwamba

7 iye adzatheratu monga momwe imatayikira ndowe yake yomwe;

8 Adzazimirira ngati maloto ndipo sadzapezekanso,

9 Diso limene linamuona silidzamuonanso;

10 Ana ake adzabwezera zonse

11 Mphamvu zaunyamata zimene zili mʼthupi mwake

12 “Ngakhale zoyipa zili zozuna mʼkamwa mwake

13 ngakhale salola kuzilavula,

14 koma chakudya chake chidzawawasa mʼmimba mwake;

15 Adzachisanza chuma chimene anachimeza;

16 Iye adzayamwa ndulu ya njoka ndipo

17 Sadzasangalala ndi timitsinje,

18 Ayenera kubweza zimene anazigwirira ntchito osazidya;

19 Pakuti iye anapondereza anthu osauka ndipo anawasiya wopanda thandizo;

20 “Chifukwa choti umbombo wake sutha,

21 Palibe chatsala kuti iye adye;

22 Ngakhale ndi munthu wachuma, mavuto adzamugwera;

23 Akadya nʼkukhuta,

24 Ngakhale athawe mkondo wachitsulo,

25 Muviwo adzawutulutsira ku msana,

26 mdima wandiweyani ukudikira chuma chake.

27 Zamumlengalenga zidzawulula kulakwa kwake;

28 Chigumula cha madzi chidzawononga nyumba yake,

29 Izi ndi zimene Mulungu amasungira anthu oyipa,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado