1 Pamenepo Bilidadi wa ku Suki anayankha kuti,
2 “Kodi iwe Yobu utsiriza liti zoyankhula zakozi?
3 Chifukwa chiyani ukutiyesa ngati ngʼombe
4 Iwe amene ukudzipweteka wekha ndi mkwiyo wako,
5 “Nyale ya munthu woyipa yazimitsidwa;
6 Kuwala kwa mʼnyumba mwake kwasanduka mdima;
7 Mayendedwe ake amgugu azilala;
8 Mapazi ake amulowetsa mu ukonde
9 Msampha wamkola mwendo;
10 Amutchera msampha pansi mobisika;
11 Zoopsa zikumuchititsa mantha kumbali zonse,
12 Mphamvu zake zatha chifukwa cha njala,
13 Wagwidwa nthenda yoopsa thupi lonse;
14 Wachotsedwa mʼnyumba imene ankadalira,
15 Mʼnyumba mwake zonse zachotsedwamo;
16 Mizu yake ikuwuma pansi
17 Sadzakumbukiridwanso pa dziko lapansi;
18 Amuchotsa pa malo owala ndi kumuponya ku mdima,
19 Iye alibe ana kapena zidzukulu pakati pa anthu ake,
20 Anthu akumadzulo adabwa kwambiri ndi tsoka lake;
21 Ndithudi, izi ndiye zimagwera munthu woyipa;