Jó 18

NYA

1 Pamenepo Bilidadi wa ku Suki anayankha kuti,

2 “Kodi iwe Yobu utsiriza liti zoyankhula zakozi?

3 Chifukwa chiyani ukutiyesa ngati ngʼombe

4 Iwe amene ukudzipweteka wekha ndi mkwiyo wako,

5 “Nyale ya munthu woyipa yazimitsidwa;

6 Kuwala kwa mʼnyumba mwake kwasanduka mdima;

7 Mayendedwe ake amgugu azilala;

8 Mapazi ake amulowetsa mu ukonde

9 Msampha wamkola mwendo;

10 Amutchera msampha pansi mobisika;

11 Zoopsa zikumuchititsa mantha kumbali zonse,

12 Mphamvu zake zatha chifukwa cha njala,

13 Wagwidwa nthenda yoopsa thupi lonse;

14 Wachotsedwa mʼnyumba imene ankadalira,

15 Mʼnyumba mwake zonse zachotsedwamo;

16 Mizu yake ikuwuma pansi

17 Sadzakumbukiridwanso pa dziko lapansi;

18 Amuchotsa pa malo owala ndi kumuponya ku mdima,

19 Iye alibe ana kapena zidzukulu pakati pa anthu ake,

20 Anthu akumadzulo adabwa kwambiri ndi tsoka lake;

21 Ndithudi, izi ndiye zimagwera munthu woyipa;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado