Jó 17

NYA

1 “Mtima wanga wasweka,

2 Ndithudi, anthu ondiseka andizungulira;

3 “Inu Mulungu, patseni chikole chimene mukufuna.

4 Inu mwatseka maganizo awo kuti asamvetse zinthu;

5 Ngati munthu apereka mnzake chifukwa cha chuma,

6 “Mulungu wandisandutsa chisudzo chochiseka aliyense,

7 Mʼmaso mwanga mwada ndi chisoni;

8 Anthu olungama akudabwa nazo zimenezi;

9 Komabe anthu olungama adzasunga njira zawo,

10 “Tsono bwerani nonsenu, bwerezaninso mawu anuwo,

11 Masiku anga atha, zimene ndinakonza zalephereka,

12 Anthu awa amasandutsa usiku kukhala usana,

13 Ngati nyumba imene ndikuyiyembekezera ndi manda,

14 ngati ndinena kwa dzenje la manda ‘ndinu abambo anga,’

15 tsono chiyembekezo changa chili kuti?

16 Ndithu sindidzakhalanso ndi chiyembekezo chilichonse,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado