Jó 16

NYA

1 Pamenepo Yobu anayankha kuti,

2 “Ndinamvapo zambiri monga zimenezi;

3 Kodi mawu anu ochulukawo adzatha?

4 Inenso ndikanatha kuyankhula monga inu,

5 Ndipo mawu a pakamwa panga akanakulimbikitsani;

6 “Koma ine ndikati ndiyankhule ululu wanga sukuchepa;

7 Ndithudi, Inu Mulungu mwanditha mphamvu;

8 Inu mwandimanga ndipo kundimangako kwakhala umboni;

9 Mulungu amabwera kwa ine mwankhanza ndipo amadana nane,

10 Anthu amatsekula pakamwa pawo kundikuwiza;

11 Mulungu wandipereka kwa anthu ochita zoyipa

12 Ine ndinali pamtendere, koma Mulungu ananditswanya;

13 anthu ake oponya mauta andizungulira.

14 Akundivulaza kawirikawiri,

15 “Ndasokerera chiguduli pa thupi langa

16 Maso anga afiira ndi kulira,

17 komatu manja anga sanachite zachiwawa

18 “Iwe dziko lapansi, usakwirire magazi anga;

19 Ngakhale tsopano mboni yanga ili kumwamba;

20 Wondipembedzera ndi bwenzi langa,

21 iye, mʼmalo mwanga, amamudandaulira Mulungu

22 “Pakuti sipapita zaka zambiri

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado