Jó 14

NYA

1 “Munthu wobadwa mwa amayi

2 Amaphuka ngati duwa ndipo kenaka amafota;

3 Kodi munthu wotereyo nʼkumuyangʼanitsitsa?

4 Ndani angatulutse chabwino mʼchoyipa?

5 Masiku a munthu ndi odziwikiratu;

6 Choncho Inu mumufulatire ndipo mumuleke apumule

7 “Mtengo uli nacho chiyembekezo:

8 Mizu yake ingathe kukalamba mʼnthaka

9 koma pamene chinyontho chafika udzaphukira

10 Koma munthu amafa nayikidwa mʼmanda,

11 Monga madzi amaphwera mʼnyanja

12 momwemonso munthu amagona ndipo sadzukanso;

13 “Aa, Inu mukanangondibisa mʼmanda

14 Munthu akafa, kodi adzakhalanso ndi moyo?

15 Inu mudzandiyitane ndipo ndidzakuyankhani;

16 Ndithudi pamenepo mudzayangʼana mayendedwe anga

17 Zolakwa zanga zidzakulungidwa mʼthumba;

18 “Koma monga phiri limakokolokera ndi kuswekasweka

19 monganso madzi oyenda amaperesera miyala

20 Inu mumamugonjetsa kamodzinʼkamodzi ndipo munthuyo nʼkutheratu;

21 Ana ake akamalemekezedwa, iyeyo sazidziwa zimenezo;

22 Iye amangomva zowawa za mʼthupi lake

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado