Isaías 65

NYA

1 “Ndinali wokonzeka kumva mapemphero a amene sankandipempha kanthu;

2 Tsiku lonse ndatambasulira manja anga

3 Ndatambasulira manja anga anthu aja amene nthawi zonse amandikwiyitsa

4 Amakatandala ku manda

5 Amawuza ena kuti, ‘Khala patali usandiyandikire,

6 “Taonani, ndatsimikiza kale mlandu ndi chilango chawo;

7 ndi a makolo awo,”

8 Yehova akuti,

9 Ndidzatulutsa zidzukulu mʼbanja la Yakobo,

10 Chigwa cha Saroni chidzakhala kodyetserako nkhosa,

11 “Koma inu amene mumasiya Yehova

12 ndidzakuperekani ku lupanga ngati nsembe,

13 Nʼchifukwa chake Ambuye Yehova akuti,

14 Atumiki anga adzayimba

15 Anthu anga osankhidwa

16 Aliyense wopempha dalitso mʼdzikomo

17 “Taonani, ndikulenga

18 Koma inu mukhale osangalala ndi okondwa mpaka muyaya

19 Ine ndidzakondwa chifuwa cha Yerusalemu

20 “Ana sadzafa ali akhanda

21 Anthu adzamanga nyumba ndi kukhalamo,

22 Sadzamanganso nyumba anthu ena nʼkukhalamo,

23 Sadzagwira ntchito pachabe

24 Ndidzawayankha ngakhale asanathe nʼkupempha komwe.

25 Mʼmbulu ndi mwana wankhosa wamkazi zidzadyera pamodzi.

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado