1 “Ndinali wokonzeka kumva mapemphero a amene sankandipempha kanthu;
2 Tsiku lonse ndatambasulira manja anga
3 Ndatambasulira manja anga anthu aja amene nthawi zonse amandikwiyitsa
4 Amakatandala ku manda
5 Amawuza ena kuti, ‘Khala patali usandiyandikire,
6 “Taonani, ndatsimikiza kale mlandu ndi chilango chawo;
7 ndi a makolo awo,”
8 Yehova akuti,
9 Ndidzatulutsa zidzukulu mʼbanja la Yakobo,
10 Chigwa cha Saroni chidzakhala kodyetserako nkhosa,
11 “Koma inu amene mumasiya Yehova
12 ndidzakuperekani ku lupanga ngati nsembe,
13 Nʼchifukwa chake Ambuye Yehova akuti,
14 Atumiki anga adzayimba
15 Anthu anga osankhidwa
16 Aliyense wopempha dalitso mʼdzikomo
17 “Taonani, ndikulenga
18 Koma inu mukhale osangalala ndi okondwa mpaka muyaya
19 Ine ndidzakondwa chifuwa cha Yerusalemu
20 “Ana sadzafa ali akhanda
21 Anthu adzamanga nyumba ndi kukhalamo,
22 Sadzamanganso nyumba anthu ena nʼkukhalamo,
23 Sadzagwira ntchito pachabe
24 Ndidzawayankha ngakhale asanathe nʼkupempha komwe.
25 Mʼmbulu ndi mwana wankhosa wamkazi zidzadyera pamodzi.