Isaías 64

NYA

1 Inu Yehova, bwanji mukanangongʼamba mlengalenga ndi kutsika pansi,

2 Monga momwe moto umatenthera tchire

3 Pakuti nthawi ina pamene munatsika munachita zinthu zoopsa zimene sitinaziyembekezere,

4 Chikhalire palibe ndi mmodzi yemwe anamvapo

5 Inu mumabwera kudzathandiza onse amene amakondwera pochita zolungama,

6 Tonsefe takhala ngati anthu amene ndi odetsedwa,

7 Palibe amene amapemphera kwa Inu

8 Komabe, Inu Yehova ndinu Atate athu.

9 Inu Yehova, musatikwiyire kopitirira muyeso

10 Mizinda yanu yopatulika yasanduka chipululu;

11 Nyumba yanu yopatulika ndi yaulemu, kumene makolo athu ankakutamandani,

12 Inu Yehova, zonse zachitikazi, kodi mungokhala osatithandiza?

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado