1 Kodi ndani uyo akubwera kuchokera ku Edomu,
2 Nanga bwanji zovala zanu zili psuu,
3 “Ndapondereza ndekha anthu a mitundu ina ngati mphesa,
4 Pakuti ndinatsimikiza mu mtima mwanga kuti lafika tsiku lolipsira anthu anga;
5 Ndinayangʼana ndipo panalibe munthu wondithandiza.
6 Ndinapondereza mitundu ya anthu ndili wokwiya;
7 Ndidzafotokoza za kukoma mtima kwa Yehova,
8 Yehova anati, “Ndithu awa ndi anthu anga,
9 Iyenso anasautsidwa mʼmasautso awo onse,
10 Komabe iwo anawukira
11 Pamenepo anthu ake anakumbukira masiku amakedzana,
12 Ali kuti amene anachita zinthu zodabwitsa
13 amene anawayendetsa pa nyanja yozama?
14 Mzimu Woyera unawapumulitsa
15 Inu Yehova amene muli kumwambako, pa mpando wanu wolemekezeka,
16 Koma Inu ndinu Atate athu,
17 Chifukwa chiyani, Inu Yehova, mukutisocheretsa pa njira zanu?
18 Anthu anu atangokhala pa malo anu opatulika pa kanthawi kochepa,
19 Ife tili ngati anthu amene