Isaías 62

NYA

1 Chifukwa chokonda Ziyoni sindidzakhala chete,

2 Mitundu ya anthu idzaona iwe utapambana pa nkhondo

3 Udzakhala ngati chipewa chaulemerero mʼdzanja la Yehova,

4 Sadzakutchanso “Wosiyidwa,”

5 Monga mnyamata amakwatira namwali,

6 Iwe Yerusalemu, pa malinga ako ndayikapo alonda;

7 Musamupatse mpata wopuma mpaka atakhazikitsa Yerusalemu

8 Yehova analumbira atakweza dzanja lake.

9 Koma amene amakakolola ndiwo amene adzadye buledi

10 Tulukani, dutsani pa zipata!

11 Yehova walengeza

12 Iwo adzatchedwa Anthu Opatulika,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado