1 Chifukwa chokonda Ziyoni sindidzakhala chete,
2 Mitundu ya anthu idzaona iwe utapambana pa nkhondo
3 Udzakhala ngati chipewa chaulemerero mʼdzanja la Yehova,
4 Sadzakutchanso “Wosiyidwa,”
5 Monga mnyamata amakwatira namwali,
6 Iwe Yerusalemu, pa malinga ako ndayikapo alonda;
7 Musamupatse mpata wopuma mpaka atakhazikitsa Yerusalemu
8 Yehova analumbira atakweza dzanja lake.
9 Koma amene amakakolola ndiwo amene adzadye buledi
10 Tulukani, dutsani pa zipata!
11 Yehova walengeza
12 Iwo adzatchedwa Anthu Opatulika,