1 Mzimu wa Ambuye Yehova uli pa ine,
2 Wandituma kuti ndikalengeze nthawi imene Yehova adzapulumutsa anthu ake;
3 Wandituma kuti ndiwakonzere olira a ku Ziyoni,
4 Adzamanganso mabwinja akale a mzinda
5 Anthu achilendo adzakutumikirani; adzazidyetsa ziweto zanu;
6 Ndipo inu mudzatchedwa ansembe a Yehova,
7 Chifukwa manyazi awo anali owirikiza;
8 “Pakuti Ine Yehova, ndimakonda chilungamo;
9 Ana awo adzakhala odziwika pakati pa mitundu ya anthu
10 Ine ndikusangalala kwambiri chifukwa cha Yehova;
11 Monga momwe nthaka imameretsa mbewu