1 “Fuwula kwambiri, usaleke.
2 Pakuti tsiku ndi tsiku amafunafuna Ine;
3 Anthu akufunsa kuti, ‘Chifukwa chiyani ife tasala
4 Mumati uku mukusala kudya, uku mukukangana ndi kumenyana,
5 Kodi kusala kudya kumene ndimakufuna Ine nʼkumeneku,
6 “Kodi si uku kusala kudya kumene Ine ndimakufuna:
7 Anthu anjala kodi mwawagawira chakudya chanu?
8 Mukatero chipulumutso chanu chidzabwera ngati mʼbandakucha,
9 Mukamadzapemphera Yehova adzakuyankhani;
10 Ndipo ngati mudyetsa anthu anjala,
11 Yehova adzakutsogolerani nthawi zonse;
12 Anthu ako adzamanganso nyumba zimene zakhala mabwinja nthawi yayitali,
13 “Muzisunga osaphwanya Sabata;
14 mukatero mudzapeza chimwemwe mwa Yehova,